Daily
Daily daily daily
Daily
Daily daily daily
Theresa Phondo
Esther Chungu
Tio mwana waku mmawa
Odi odi I’m calling
Nikuti konkonko
Olo kodi when I am falling
Yesu enkonto iyo
Jehovah (Jehovah)
Alinaiwe, mu BM olo Benz
Or njinga uma chova
(Jehovah)
Ali na iwe
Ali na ine eh
Dai-dai-daily
Atuma angelo asamale ine
Dai-dai-daily
Ndikasochera andilondolera
Dai-dai-daily
Atuma angelo asamale ine eh, eh
Daily daily
Sangandisiye ndekha
Sangandi ponye ponye paliponse
Sangandisiye ndekha
Andimenyela nkhondo zakumdima
Sangandisiye ndekha
Sangandi ponye ponye paliponse
Sangandisiye ndekha
Andimenyela nkhondo zakumdima
Dai-dai-daily
Dai-dai-daily
Dai-dai-daily
Dai-dai-daily
Dai-dai-daily
Anikonda Yesu yo (yelele yelele)
Samagona pali ineh
Ani sunga Yesu yo (yelele yelele)
Anafa kuti ninkale na umoyo
I am blessed and favored oh
(Blessed and favored oh)
I’m a child of the King
Peace and joy on overflow
(Joy on overflow)
Ndine okondewa
Satopa kundiyang’anira
Usiku ndi usana kundisamalira
My Lord and Savior Yesu yo Yesu yo inu Yesu yo
Satopa kundiyang’anira
Usiku ndi usana kundisamalira
My Lord and Savior Yesu yo Yesu yo Yesu yo oh
Dai-dai-daily
Atuma angelo asamale ine
Dai-dai-daily
Ndikasochera andilondolera
Dai-dai-daily
Atuma angelo asamale ine
Daily daily
Sangandisiye ndekha
Sangandi ponye ponye paliponse
Sangandisiye ndekha
Andimenyela nkhondo zakumdima
Sangandisiye ndekha
Sangani ponye ponye paliponse
Sangandisiye ndekha
Andimenyela nkhondo zakumdima
Dai-dai-daily
Hey daily daily oh
Daily daily oh
Dai-dai-daily
Daily daily oh
Daily daily oh
Dai-dai-daily
Sangandisiye ndekha
Sangandisiye ndekha
Daily daily oh
Daily daily oh